Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsamba 3
  • Anasiya Kuchita Zimene Mulungu Ankafuna

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anasiya Kuchita Zimene Mulungu Ankafuna
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Yeremiya—Mneneri Wachilendo wa Ziweruzo za Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Khalani Olimba Mtima Ngati Yeremiya
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • “Ndaika Mawu Anga M’kamwa Mwako”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Yeremiya Sanasiye Kulankhula za Yehova
    Phunzitsani Ana Anu
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 March tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 5-7

Anasiya Kuchita Zimene Mulungu Ankafuna

7:1-4, 8-10, 15

  • Yeremiya anaulula molimba mtima machimo ndiponso chinyengo cha Aisiraeli

  • Aisiraeli ankaganiza kuti kachisi ali ndi mphamvu inayake yapadera yoti ingawateteze

  • Yehova anawauza kuti nsembe zimene ankapereka mwamwambo sizingachotse machimo awo

Dzifunseni kuti: Kodi ndingatani kuti ndizilambira Yehova mogwirizana ndi zimene amafuna osati mwamwambo chabe?

Yeremiya akulengeza uthenga wa Yehova ataima pachipata cha kachisi

Yeremiya waima pachipata cha nyumba ya Yehova

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena