Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsamba 4
  • Fanizo la Msamariya Wachifundo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Fanizo la Msamariya Wachifundo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Kukhala “Msamariya Wachifundo” Kumatanthauza Chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Msamariya Apezeka Kuti Ndiye Mnansi Wabwino
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Fanizo la Mwana Wolowerera
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 July tsamba 4
Msamariya wachifundo akumanga mabala a Myuda yemwe wavulazidwa

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LUKA 10-11

Fanizo la Msamariya Wachifundo

10:25-37

Yesu ananena fanizoli pamene ankayankha funso lakuti, “Nanga mnzanga amene ndikuyenera kumukonda ndani kwenikweni?” (Luka 10:25-29) Iye ankadziwa kuti mpingo wachikhristu udzapangidwa ndi anthu “osiyanasiyana” kuphatikizapo Asamariya komanso anthu a mitundu ina. (Yoh. 12:32) Fanizoli linathandiza otsatira ake kuti aziyesetsa kuchita zonse zomwe angathe kuti azikonda ena, ngakhale omwe amasiyana nawo m’zinthu zambiri.

Anthu a mitundu yosiyanasiyana akusangalalira limodzi

DZIFUNSENI KUTI:

  • ‘Kodi ndimawaona bwanji abale ndi alongo a zikhalidwe zina?’

  • ‘Kodi ndimakonda kucheza ndi anthu okhawo omwe ndimafanana nawo m’zinthu zambiri?’

  • ‘Kodi pali zimene ndingachite kuti ndidziwane bwino ndi Akhristu ochokera m’mayiko ena komanso zikhalidwe zosiyanasiyana?’ (2 Akor. 6:13)

Kod ndi ndani amene ndikufuna kuti . . .

  • adzalowe nane mu utumiki?

  • abwere kudzadya kunyumba kwathu?

  • abwere kwathu kudzachita nawo Kulambira kwa Pabanja?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena