Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 March tsamba 6
  • “Chofufumitsa Chaching’ono Chimafufumitsa Mtanda Wonse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chofufumitsa Chaching’ono Chimafufumitsa Mtanda Wonse”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kuchotsa Anthu Osalapa Kumathandiza
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Chifukwa Chake Kuchotsa Kuli Makonzedwe Achikondi
    Galamukani!—1996
  • Munthu Amene Mumamukonda Akasiya Kutumikira Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Timasonyeza Chikondi Tikamachita Zinthu Mogwirizana Ndi Chilango Chochokera kwa Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 March tsamba 6
Munthu wochotsedwa akutuluka m’Nyumba ya Ufumu misonkhano itangotha; akuona abale ndi alongo akucheza mosangalala

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 AKORINTO 4-6

“Chofufumitsa Chaching’ono Chimafufumitsa Mtanda Wonse”

5:1, 2, 5-11, 13

Munthu akachotsedwa mumpingo zimakhala zopweteka kwambiri. Ndiye n’chifukwa chiyani tinganene kuti kuchita zimenezi kumasonyeza chikondi?

Tingatero chifukwa kuchotsa munthu . . .

  • kumasonyeza kuti timakonda Yehova chifukwa kumalemekeza dzina lake loyera.​—1 Pet. 1:15, 16

  • kumasonyeza kuti timakonda abale ndi alongo chifukwa kumawateteza kuti asatengere makhalidwe oipa.​—1 Akor. 5:6

  • kumasonyeza kuti timakonda wolakwayo chifukwa kumamuthandiza kuzindikira kulakwa kwake kuti alape.​—Aheb. 12:11

Kodi tingathandize bwanji Akhristu omwe ali ndi wachibale wochotsedwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena