Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 April tsamba 6
  • Mulungu Adzakhala “Zinthu Zonse kwa Aliyense”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mulungu Adzakhala “Zinthu Zonse kwa Aliyense”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Kodi N’kusungiranji Malonjezo Anu?
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Mtendere Udzayamba mu Ulamuliro wa Zaka 1,000
    Nsanja ya Olonda—2012
  • “Khalani Oyera”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 April tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 AKORINTO 14-16

Mulungu Adzakhala “Zinthu Zonse kwa Aliyense”

15:24-28

Anthu amene ndi okhulupirika kwa Yehova adzakhala ndi tsogolo labwino kwambiri. Tikamafotokozera ena zinthu zosangalatsa zomwe tikuyembekezera sitikayikira kuti zidzachitikadi. Mtumwi Paulo analimbikitsa Akhristu anzake kuti aziyerekezera mmene zidzakhalire kumapeto Ulamuliro wa Zaka 1,000 wa Khristu pamene Yehova adzakhale “zinthu zonse kwa aliyense.”

Angelo akuteteza anthu a Yehova pa chisautso chachikulu; anthu ali m’paradaiso; Yesu akuchotsa chisoti chake chachifumu n’kupereka ufumu kwa Yehova Mulungu

Ndi chiyembekezo chiti chomwe chimakusangalatsani kwambiri ndipo n’chifukwa chiyani?

N’chiyani chimakutsimikizirani kuti zimene Mulungu analonjeza zidzakwaniritsidwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena