Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 3
  • ‘Chithunzi cha Zinthu Zabwino Zimene Zikubwera’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Chithunzi cha Zinthu Zabwino Zimene Zikubwera’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Chinthu Chofunika Kwambiri M’chihema
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Muziyamikira Mwayi Wanu Wolambira M’kachisi Wauzimu wa Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Chihema Cholambiriramo
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • ‘Munagulidwa ndi Mtengo’
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AHEBERI 9-10

‘Chithunzi cha Zinthu Zabwino Zimene Zikubwera’

9:12-14, 24-26; 10:1-4

Chihema chinkaimira zimene Mulungu anakonza zoti adzakhululukire anthu machimo awo onse pogwiritsa ntchito nsembe ya Yesu. Gwirizanitsani zinthu 4 za pachihema ndi zimene zinkaimira.

Chithunzi chosonyeza mmene mkati mwa chihema munkaonekera
  1. Nsalu yotchinga

  2. Kuwaza magazi a nyama patsogolo pa guwa la nsembe

  3. Malo Oyera Koposa

  4. Mkulu wa ansembe

  • Yesu

  • Kumwamba

  • Kukapereka mtengo wa nsembe yake kwa Yehova

  • Thupi la Khristu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena