CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AHEBERI 9-10
‘Chithunzi cha Zinthu Zabwino Zimene Zikubwera’
Chihema chinkaimira zimene Mulungu anakonza zoti adzakhululukire anthu machimo awo onse pogwiritsa ntchito nsembe ya Yesu. Gwirizanitsani zinthu 4 za pachihema ndi zimene zinkaimira.
|
|