Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsamba 4
  • Chinthu Chofunika Kwambiri M’chihema

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chinthu Chofunika Kwambiri M’chihema
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Chithunzi cha Zinthu Zabwino Zimene Zikubwera’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Kodi Likasa la Pangano N’chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Chihema Cholambiriramo
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 September tsamba 4
Likasa la pangano.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 25-26

Chinthu Chofunika Kwambiri M’chihema

25:9, 21, 22

Likasa linali chinthu chofunika kwambiri m’chihema komanso mumsasa wonse wa Aisiraeli. Mtambo umene unkakhala pakati pa akerubi awiri pamwamba pa chivundikiro chophimba machimo cha Likasa unkaimira kukhalapo kwa Mulungu. Chaka chilichonse pa Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo, mkulu wa ansembe ankalowa m’Malo Oyera Koposa n’kudontheza magazi a ng’ombe yamphongo ndiponso a mbuzi patsogolo pa chivundikiro kuti aphimbe machimo a Aisiraeli. (Le 16:14, 15) Zimenezi zinkaimira pamene Yesu, yemwe ndi Mkulu wa Ansembe wamkulu, anakaonekera kwa Yehova kumwamba kuti apereke nsembe ya dipo.​—Ahe 9:24-26.

Gwirizanitsani malemba otsatirawa ndi madalitso amene tingapeze chifukwa cha dipo.

MALEMBA

  • 1Yo 1:8, 9

  • Ahe 9:13, 14

  • Aro 6:23

MADALITSO

  • chiyembekezo chodzakhala ndi moyo wosatha

  • kukhululukidwa machimo athu

  • chikumbumtima choyera

Kodi tiyenera kuchita chiyani kuti tipeze madalitso amenewa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena