Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 November tsamba 8
  • Yehova Amadziwa Zimene Timafunikira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amadziwa Zimene Timafunikira
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amasonkhanitsa Anthu Ake Osangalala
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Misonkhano Yachigawo Imatipatsa Mwayi Wosonyezana Chikondi
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Misonkhano Imene Imatilimbikitsa “pa Chikondi Ndi Ntchito Zabwino”
    Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
  • Kusonkhana Kuti Tilambire Mulungu
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 November tsamba 8
Alongo akuomba m’manja pamsonkhano wachigawo

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Yehova Amadziwa Zimene Timafunikira

Kapolo wokhulupirika ndi wanzeru amatipatsa chakudya “pa nthawi yoyenera.” Zimenezi ndi umboni wakuti Yehova amene akutsogolera kapoloyu amadziwa zimene timafunikira pa moyo wathu wauzimu. (Mat. 24:45) Misonkhano yachigawo komanso misonkhano yathu yamkati mwa mlungu, ndi zina zomwe zimatitsimikizira zimenezi.

ONERANI VIDIYO YAKUTI LIPOTI LA KOMITI YOPHUNZITSA LA 2017, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Sitediyamu yodzaza ndi anthu omwe akuchita msonkhano

    Kodi ndani amene ayenera kulemekezedwa chifukwa cha misonkhano yachigawo ya pa nthawi yake yomwe timasangalala nayo, ndipo n’chifukwa chiyani?

  • Kodi ntchito yokonzekera msonkhano wachigawo imayamba liti?

  • Abale a m’dipatimenti yojambula mavidiyo akujambula vidiyo ya pamsonkhano

    Kodi nkhani za pamsonkhano wachigawo zimasankhidwa bwanji?

  • Kodi pamakhala ntchito yotani pokonza msonkhano wachigawo?

  • Kodi njira zophunzitsira ku sukulu ya Giliyadi zimagwiritsidwa ntchito bwanji pokonza misonkhano ya mkati mwa mlungu?

  • M’bale akuwerenga ndandanda ya Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu

    Kodi madipatimenti osiyanasiyana amathandizana bwanji pokonza ndandanda yautumiki?

Kodi inuyo mumachita zotani poyamikira zinthu zauzimu zomwe Yehova amatipatsa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena