Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 February tsamba 1
Abulahamu akuphunzitsa Isaki zokhudza Yehova ndipo akumulozera nyenyezi. Sara waima chapatali n’kumawayang’ana.

Abulahamu akuphunzitsa Isaki zokhudza Yehova

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi tingadziwe bwanji zinthu zomwe zidzachitike m’tsogolo?

Lemba: Yes. 46:10

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi ndi maulosi a m’Baibulo ati amene akukwaniritsidwa masiku ano?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku la ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa.’ Kabuku ka ‘Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu’

    bhs 29 ¶2

  • fg phunziro 3 ¶2

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: Kodi ndi maulosi a m’Baibulo ati amene akukwaniritsidwa masiku ano?

Lemba: 2 Tim. 3:1-5

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi anthu adzasangalala ndi madalitso ati m’dziko limene Mulungu walonjeza?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku la ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa.’ Kabuku ka ‘Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu’

    bhs 98 ¶10

  • fg phunziro 1 ¶3

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi anthu adzasangalala ndi madalitso ati m’dziko limene Mulungu walonjeza?

Lemba: Yes. 65:21-23

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Yesu ali ndi udindo wotani pokwaniritsa zimene Mulungu analonjeza?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku la ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa’

    bhs 35 ¶20

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena