Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 January tsamba 1
Nowa ndi banja lake akukonzekera kulowa m’chingalawa

Nowa ndi banja lake akukonzekera kulowa m’chingalawa

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi Mulungu dzina lake ndi ndani?

Lemba: Sal. 83:18

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi khalidwe lalikulu la Mulungu ndi chiyani?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • The book ‘What Can the Bible Teach Us?’ and the brochure ‘Good News From God!’

    bhs 12 ¶14

  • fg phunziro 2

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: Kodi khalidwe lalikulu la Mulungu ndi chiyani?

Lemba: 1 Yoh. 4:8

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi munthu angatani kuti akhale bwenzi la Mulungu?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • The book ‘What Can the Bible Teach Us?’ and the brochure ‘Listen to God and Live Forever.’

    bhs 11 ¶13

  • ll 29

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi munthu angatani kuti akhale bwenzi la Mulungu?

Lemba: Yoh. 17:3

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Yehova amatithandiza bwanji kudziwa zomwe zidzachitike m’tsogolo?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • The book ‘What Can the Bible Teach Us?’ and the brochure ‘Good News From God!’

    bhs 15 ¶19

  • fg phunziro 3

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena