Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 November tsamba 16
  • Muzilola Kuti Yehova Azikuthandizani Kudzera M’pemphero

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzilola Kuti Yehova Azikuthandizani Kudzera M’pemphero
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Mungachite Kuti Muzisangalala Kwambiri Mu Utumiki​—Muzifunsa Mafunso
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Mungachite Kuti Muzisangalala Kwambiri mu Utumiki
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Muziwafika Pamtima
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Muzithandiza Ophunzira Baibulo Kuti Asiye Makhalidwe Oipa
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 November tsamba 16

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI | ZIMENE MUNGACHITE KUTI MUZISANGALALA KWAMBIRI MU UTUMIKI

Muzilola Kuti Yehova Azikuthandizani Kudzera M’pemphero

Yehova ndi amene amachititsa kuti mbewu ya choonadi imere komanso ikule mumtima mwa munthu. (1Ak 3:6-9) Choncho kuti zinthu zizitiyendera bwino mu utumiki, tiyenera kudalira Yehova kuti azitithandiza komanso kuti azithandiza anthu amene timaphunzira nawo Baibulo.

Muzipempha Yehova kuti azithandiza ophunzira anu kupirira mavuto komanso kulimbana ndi mayesero. (Afi 1:9, 10) Muzitchula zimenezi mwachindunji. Muzipemphera kuti mzimu woyera uzitsogolera maganizo komanso zochita zanu. (Lu 11:13) Muziphunzitsa ophunzira anu kupemphera ndipo muziwalimbikitsa kuti azitero. Muziwapempherera ophunzira anu komanso muzipemphera nawo limodzi ndipo muzitchula dzina lawo.

ONERANI VIDIYO YAKUTI MUZIGWIRITSA NTCHITO ZOMWE YEHOVA WATIPATSA KUTI MUZISANGALALA NDI NTCHITO YOPHUNZITSA​—PEMPHERO, NDIPO KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi Anita anakumana ndi vuto lotani pamene ankaphunzira ndi Jane?

  • Kodi lemba la 1 Akorinto 3:6 linamuthandiza bwanji Anita?

  • Kodi vuto lomwe Anita anakumana nalo linatha bwanji?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena