Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 January tsamba 15
  • Sauli Anali Wodzichepetsa Poyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Sauli Anali Wodzichepetsa Poyamba
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Kudzikuza Kumabweretsa Manyazi
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • “Kumvera Kuposa Nsembe”
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Kumvera Kumaposa Nsembe
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Yesu Anasankha Saulo
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 January tsamba 15

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Sauli Anali Wodzichepetsa Poyamba

Sauli anali wodzichepetsa ndipo anazengereza kuti avomere ufumu (1Sa 9:21; 10:20-22; w20.08 10 ¶11)

Sauli sankachita zinthu mwaphuma anthu ena akamulankhula mwachipongwe (1Sa 10:27; 11:12, 13; w14 3/15 9 ¶8)

Sauli ankatsatira malangizo a mzimu woyera wa Yehova (1Sa 11:5-7; w95 12/15 10 ¶1)

Mkulu akusonyeza mlongo yemwe wanyamula khadi la ukwati lemba la m’Baibulo.

Kudzichepetsa kudzatithandiza kuti tiziona mwayi wathu wa utumiki komanso zomwe timakwanitsa kuchita kuti ndi mphatso zochokera kwa Yehova. (Aro 12:3, 16; 1Ak 4:7) Ndiponso ngati tili odzichepetsa, tidzapitiriza kudalira Yehova kuti azititsogolera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena