Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsamba 11
  • Muzitsanzira Mmene Yehova Amagwiritsira Ntchito Udindo Wake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzitsanzira Mmene Yehova Amagwiritsira Ntchito Udindo Wake
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Chilamulo Chinkasonyeza Bwanji Kuti Yehova Amaganizira Anthu Osauka?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Anagwiritsa Ntchito Udindo Wake Pothandiza Anthu Ena
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Mfundo Zothandiza Kuweruza Milandu Mwachilungamo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Anagwira Ntchito Mwamphamvu Komanso ndi Mtima Wonse
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 September tsamba 11

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzitsanzira Mmene Yehova Amagwiritsira Ntchito Udindo Wake

Yehova ndi wolamulira wamkulu (1Mf 22:19; it-2 21)

Yehova amalemekeza amene amawalamulira (1Mf 22:20-22; w21.02 4 ¶9)

Yehova anadalitsa zomwe mngelo anachita (1Mf 22:23; it-2 245)

Bambo akuchititsa kulambira kwa pabanja ndi mkazi komanso mwana wake. Akumwetulira pamene mwana wake akufotokoza.

Akulu komanso mitu ya mabanja ayenera kutsanzira mmene Yehova amagwiritsira ntchito udindo. (Aef 6:4; 1Pe 3:7; 5:2, 3) Akamachita zimenezi anthu amene amawayang’anira amakhala osangalala.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena