Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 March tsamba 4
  • Malangizo Achikondi a Bambo Opita kwa Mwana Wake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malangizo Achikondi a Bambo Opita kwa Mwana Wake
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Muzithandiza Achinyamata Kuti Azichita Zambiri
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Muzikhala Wofunitsitsa Kuchita Zimene Mulungu Amafuna
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Yehova Amaona Kuti Moyo wa Munthu Ndi Wamtengo Wapatali
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Thawirani kwa Yehova
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 March tsamba 4
Zithunzi: 1. Mfumu Davide yemwe tsopano wakalamba, akukambirana ndi Solomo mapulani omangira kachisi. 2. Mfumu Solomo ikutsogolera ntchito yomanga kachisi.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Malangizo Achikondi a Bambo Opita kwa Mwana Wake

Um’dziwe bwino Yehova (1Mb 28:9; w05 2/15 19 ¶9)

Um’tumikire Yehova ndi mtima wathunthu (1Mb 28:9; w12 4/15 16 ¶13)

Uzidalira Yehova ndipo usachite mantha (1Mb 28:20; w17.09 32 ¶20-21)

Mfumu Davide yemwe panthawiyi anali wachikulire, anapereka malangizo amenewa kwa mwana wake Solomo amene anali wosadziwa zambiri pamene ankafuna kuyamba kugwira ntchito yofunika kwambiri yomanga kachisi. N’chifukwa chiyani malangizo amenewa ali ofunika kwambiri kwa aliyense, koma makamaka achinyamata Achikhristu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena