Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 January tsamba 12
  • Zinthu Zimatiyendera Bwino Tikamatsatira Malangizo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zinthu Zimatiyendera Bwino Tikamatsatira Malangizo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Malangizo Achikondi a Bambo Opita kwa Mwana Wake
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Kodi Likasa la Pangano N’chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Kodi Chilamulo Chinkasonyeza Bwanji Kuti Yehova Amaganizira Zinyama?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Muzikhalabe Wosangalala Ngakhale Pamene Zinthu Sizikuyenda Bwino
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 January tsamba 12
Mfumu Davide limodzi ndi Aisiraeli ena akuimba komanso kuvina pamene Alevi anyamula likasa la pangano.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zinthu Zimatiyendera Bwino Tikamatsatira Malangizo

Davide ankafuna kuti likasa la pangano libwerere ku Yerusalemu (1Mb 13:3)

Pa ulendo woyamba zinakanika atalola kuti likasalo linyamulidwe m’njira yosayenera (1Mb 15:13; w03 5/1 10-11)

Davide atafufuza malangizo a Yehova, zinthu zinamuyendera bwino (1Mb 15:2; 16:11; w03 5/1 11 ¶13)

Yehova amayamikira tikamachita zinthu ndi zolinga zabwino. Komabe, kuti azisangalala ndi zochita zathu tiyenera kumatsatira malangizo ake.​—De 30:16.

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena