Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 May tsamba 2
  • Muziona Ena Mmene Yehova Amawaonera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muziona Ena Mmene Yehova Amawaonera
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • “Khulupirirani Yehova Mulungu Wanu”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Yehosafati Adalira Yehova
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • Yehova Anathandiza Mfumu Yehosafati
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kodi Mumatsatira ndi Mtima Wonse Zimene Zinalembedwa?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 May tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muziona Ena Mmene Yehova Amawaonera

Mfumu Yehosafati inachita zinthu mopanda nzeru pamene inapanga mgwirizano ndi Mfumu Ahabu (2Mb 18:1-3; w17.03 24 ¶7)

Yehova anatumiza Yehu kuti akadzudzule Yehosafati (2Mb 19:1, 2)

Yehova anakumbukira zinthu zabwino zimene Yehosafati anachita (2Mb 19:3; w15 8/15 11-12 ¶8-9)

M’bale akuyang’ana moipidwa m’bale wina amene akucheza ndi anthu ena m’malo momayeretsa Nyumba ya Ufumu.

DZIFUNSENI KUTI, ‘M’malo momangoganizira zinthu zimene abale ndi alongo anga amalakwitsa, kodi ndimaona makhalidwe awo abwino ngati mmene Yehova amachitira?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena