Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 8
  • ‘Kodi Munthu Angakhale Waphindu kwa Mulungu?’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Kodi Munthu Angakhale Waphindu kwa Mulungu?’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Musamatsanzire Elifazi Potonthoza Ena
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Pewani Maganizo Olakwika
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Samalani ndi Nkhani Zabodza
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Yobu Afupidwa Chifukwa Chokhulupirika
    Nsanja ya Olonda—1998
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 8

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

‘Kodi Munthu Angakhale Waphindu kwa Mulungu?’

Elifazi ananena kuti Mulungu amaona kuti ndife opanda phindu (Yob 22:​1, 2; w05 9/15 27 ¶1-3)

Elifazi ananenanso kuti Mulungu alibe nazo ntchito zoti ndife olungama kapena ayi (Yob 22:3; w95 2/15 27 ¶6)

Zochita zathu zingachititse kuti Yehova ayankhe Satana yemwe amamutonza (Miy 27:11; w03 4/15 14-15 ¶10-12)

Mlongo wachikulire akugogoda pakhomo pamene ali mu utumiki.

FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi mumamva bwanji mukaganizira kuti Wamphamvuyonse amakuonani kuti ndinu wofunika?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena