Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 13
  • Zochita Zanga Zimathandiza Kuti Gulu Lathu Likhale ndi Mbiri Yabwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochita Zanga Zimathandiza Kuti Gulu Lathu Likhale ndi Mbiri Yabwino
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Zosankha Zomwe Zimasonyeza Kuti Timadalira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Zimene Inuyo Mwachita
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Muziwerenga Baibulo Tsiku Lililonse Komanso Muzifunafuna Nzeru
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Tizivomereza Modzichepetsa Kuti Sitikudziwa Zonse
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 13

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Zochita Zanga Zimathandiza Kuti Gulu Lathu Likhale ndi Mbiri Yabwino

Anthu amaona zimene a Mboni za Yehovafe timachita. (1Ak 4:9) Tingadzifunse kuti, ‘Kodi zochita ndi zolankhula zanga zimachititsa kuti Yehova alemekezedwe?’ (1Pe 2:12) Timayesetsa kuti tisachite chilichonse chimene chingawononge mbiri yabwino imene a Mboni za Yehova akhala nayo kwa zaka zambiri.—Mla 10:1.

Mu zochitika zotsatirazi, lembani zimene Mkhristu angachite komanso mfundo ya m’Baibulo imene ingamuthandize:

  • Munthu wosakhulupirira akakunyozani

  • Zovala zanu kapena galimoto yanu ikada, kapenanso pakhomo panu pakakhala posasamalika

  • Ngati m’dziko lanu akhazikitsa lamulo limene ndi lokondera kapena lovuta kulitsatira

Zithunzi za muvidiyo yakuti “Kuthandiza Anthu Kukonda Komanso Kulemekeza Choonadi.” 1. M’bale akuwerenga buku. 2. M’bale ndi mlongo akuona zinthu zogwiritsa ntchito pofufuza. 3. Mpukutu wa mapepala uli pafupi ndi kabuku kakuti “Mmene Moyo Unayambira​—⁠Mafunso 5 Ofunika Kwambiri.” 4. Mzimayi watsegula webusaiti ya jw.org pafoni yake.

Kodi abale ndi alongo amene amagwira ntchito yofufuza m’Dipatimenti Yolemba amachita zotani kuti gulu lathu likhale ndi mbiri yabwino?

ONERANI VIDIYO YAKUTI KUTHANDIZA ANTHU KUKONDA KOMANSO KULEMEKEZA CHOONADI, KENAKO YANKHANI FUNSO LOTSATIRALI:

Kodi chimakuchititsani chidwi n’chiyani mukaganizira khama limene gulu limachita poyesetsa kuti lifalitse nkhani zolondola?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena