Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 20
  • Kodi Mulungu Ndi Amene Amachititsa Kuti Tizivutika?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mulungu Ndi Amene Amachititsa Kuti Tizivutika?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • N’chifukwa Chiyani Anthu Akuvutika Chonchi?
    Galamukani!—2011
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2020
  • Funso Lachitatu: N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Ndizivutika?
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 20
Munthu akuthandiza munthu wina amene akuvutika

Kodi Mulungu Ndi Amene Amachititsa Kuti Tizivutika?

Yankho la m’Baibulo

Baibulo limayankha mosapita m’mbali kuti ayi. Yehova Mulungu sanalenge anthu kuti azivutika. Koma anthu awiri oyambirira, Adamu ndi Hava, anakana kugonjera ulamuliro wa Mulungu n’kumayendera mfundo zawozawo pa nkhani yokhudza zinthu zabwino ndi zoipa. Iwo anasankha kusamvera Mulungu ndipo anayamba kuvutika.

Masiku ano tikuvutikanso chifukwa choti Adamu ndi Hava anasankha kusamvera Mulungu. Koma si Mulungu amene anachititsa kuti anthufe tizivutika.

Baibulo limati, “Munthu akakhala pa mayesero asamanene kuti: ‘Mulungu akundiyesa.’ Pakuti Mulungu sangayesedwe ndi zinthu zoipa ndipo iye sayesa munthu ndi zinthu zoipa.” (Yakobo 1:13) Choncho munthu wina aliyense amavutika, ngakhale amene Mulungu amamukonda.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena