Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 July tsamba 4
  • Kodi Mungachite Upainiya kwa Chaka Chimodzi?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungachite Upainiya kwa Chaka Chimodzi?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Apainiya Amapereka ndi Kulandira Madalitso
    Nsanja ya Olonda—1994
  • “Upainiya Ungakuyenereni Kwabasi!”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Aliyense Amalimbikitsidwa
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Upainiya Umalimbitsa Ubwenzi Wathu Ndi Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2013
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 July tsamba 4

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kodi Mungachite Upainiya kwa Chaka Chimodzi?

Abale awiri akuwerengera lemba munthu wina panyumba yake

Kodi mungapeze madalitso otani ngati mutachita upainiya?​—Miy. 10:22.

MUKAMACHITA UPAINIYA, MUKHOZA KUPEZA MADALITSO OTSATIRAWA:

  • Mukhoza kukhala ndi luso lolalikira ndipo mungamasangalale mu utumiki.

  • Mungamakonde kwambiri Yehova. Mukamauza ena zokhudza Yehova m’pamenenso mumaganizira kwambiri za makhalidwe ake abwino.

  • Mungaone ubwino woika zinthu za Ufumu pamalo oyamba m’malo mwa zofuna zanu. Mungakhalenso osangalala mukamagwiritsa ntchito nthawi komanso zinthu zanu pothandiza ena mu utumiki.​—Mat. 6:33; Mac. 20:35

  • Mukhoza kulowa Sukulu ya Apainiya, kuchita nawo msonkhano wa apainiya womwe umachitika msonkhano wadera ukayandikira komanso womwe woyang’anira dera amachititsa akamachezera mpingo.

  • Mungapeze anthu ambiri oti muziphunzira nawo Baibulo.

  • Mungamakhale nthawi yaitali muli ndi abale ndi alongo, omwe angakulimbikitseni komanso kukuthandizani.​—Aroma 1:11, 12

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena