Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsamba 4
  • Wosamvera Malamulo Adzaonekera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Wosamvera Malamulo Adzaonekera
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kuzindikira “Munthu Wosayeruzika”
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • “Khalanibe Maso”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Chiweruzo cha Mulungu Motsutsana ndi “Munthu Wosayeruzika”
    Nsanja ya Olonda​—1990
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 July tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 ATESALONIKA 1-3

Wosamvera Malamulo Adzaonekera

2:6-12

Kodi Paulo ankanena za chiyani m’mavesi amenewa?

  • Akhristu ampatuko akusokoneza misonkhano m’nthawi ya atumwi

    ‘Chinachititsa kuti asaonekere’ (vesi 6)​—Zikuoneka kuti anali atumwi

  • ‘Anaonekera’ (vesi 6)​—Pambuyo poti atumwi onse amwalira, Akhristu ampatuko anayamba kuphunzitsa zinthu zabodza komanso ankachita zachinyengo

  • “Chinsinsi cha kusamvera malamulo” (vesi 7)​—M’nthawi ya Paulo, anthu sankadziwa bwinobwino kuti “wosamvera malamuloyo” ndi ndani

  • Gulu la atsogoleri azipembedzo likunyoza m’bale amene wanyamula Baibulo m’manja

    ‘Wosamvera malamulo’ (vesi 8)​—Masiku ano, wosamvera malamulo ameneyu ndi atsogoleri azipembedzo onse pamodzi

  • “Ambuye Yesu adzamuthetsa [wosamvera malamuloyo] . . . pa nthawi imene kukhalapo kwa Yesuyo kudzaonekere” (vesi 8)​—Yesu adzasonyeza kuti iyeyo ndi mfumu akadzayamba kupereka chiweruzo kudziko la Satanali kuphatikizapo ‘wosamvera malamulo’

Kodi mavesiwa akuthandizani bwanji kuti muzilalikira modzipereka komanso mwachangu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena