Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 February tsamba 5
  • Anthu Okhulupirika Amatsatira Malangizo a Gulu la Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu Okhulupirika Amatsatira Malangizo a Gulu la Yehova
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Nehemiya Anali Woyang’anira Wabwino
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Mwapatulidwa
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Madyerero Osaiŵalika a m’Mbiri ya Israyeli
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 February tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | NEHEMIYA 9-11

Anthu Okhulupirika Amatsatira Malangizo a Gulu la Yehova

Banja la Aisiraeli likumanga msasa kuti lizikhalamo panthawi ya Chikondwerero cha Misasa

Anthu okhulupirika anatsatira malangizo osiyanasiyana a gulu la Yehova

10:28-30, 32-39; 11:1, 2

  • Anthu a Yehova anakonzekera Chikondwerero cha Misasa ndipo anachita motsatira malangizo

  • Tsiku lililonse anthu ankasonkhana kuti amvetsere Chilamulo cha Mulungu ndipo ankasangalala

  • Anthu anaulula machimo, anapemphera komanso anapempha Yehova kuti awadalitse

  • Anthu anavomereza kuti apitiriza kutsatira malangizo ochokera kwa Yehova

• Anatsatira malangizo a gulu la Yehova pochita zinthu izi:

  • Mwamuna ndi mkazi wake ndipo onse amalambira Yehova

    Ankakwatirana ndi anthu okhawo amene ankalambira Yehova

  • Ndalama ziwiri zachitsulo

    Ankapereka ndalama zothandizira pa kulambira koona

  • Mpukutu womwe munali Chilamulo cha Mose

    Ankasunga Sabata

  • Nkhuni za paguwa la nsembe

    Ankapereka nkhuni zomwe ankazigwiritsa ntchito paguwa lansembe

  • Mbewu zoyamba kucha ndi mwana wa nkhosa woyamba kubadwa

    Ankapereka kwa Yehova mbewu zoyamba kucha ndiponso ziweto zoyamba kubadwa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena