Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 March tsamba 3
  • Esitere Anasonyeza Kuti Sanali Wodzikonda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Esitere Anasonyeza Kuti Sanali Wodzikonda
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Anachita Zinthu Mwanzeru, Molimba Mtima Ndiponso Moganizira Ena
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • Anachita Zinthu Mwanzeru, Molimba Mtima Ndiponso Moganizira Ena
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Analimba Mtima Kuteteza Anthu a Mulungu
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • Analimba Mtima Kuteteza Anthu a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 March tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | ESITERE 6-10

Esitere Anasonyeza Kuti Sanali Wodzikonda

Losindikizidwa

Esitere anasonyeza kuti ndi wolimba mtima komanso wosadzikonda poteteza anthu a Yehova

8:3-5, 9

  • Moyo wa Esitere ndi Moredekai sunali pangozi. Koma lamulo la Hamani loti Ayuda onse aphedwe n’kuti likulengezedwa mu ufumu wonse wa Ahasiwero

  • Esitere anaika moyo wake pangozi pokaonekeranso pamaso pa mfumu asanaitanidwe. Iye analira n’kupempha mfumuyo kuti isinthe lamulo limene Hamani anakhazikitsa

  • Malamulo operekedwa m’dzina la mfumu sankasinthidwa. Choncho mfumuyo inapatsa mphamvu Esitere ndi Moredekai kuti apange lamulo latsopano

Yehova anathandiza anthu ake kuti apambane

8:10-14, 17

  • Lamulo lachiwiri linalengezedwa ndipo linapatsa Ayuda mphamvu yoti adziteteze

  • Anthu okwera pa mahatchi anatumizidwa m’zigawo zonse za ufumuwo kuti akakonzekeretse Ayuda kumenya nkhondo

  • Anthu ambiri anaona kuti Yehova amakonda anthu ake ndipo ena anayamba kutsatira chipembedzo cha Ayuda

Esitere akumvetsera pamene Moredekai akufotokozera mlembi lamulo latsopano
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena