Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 12
  • Chuma Chapadera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chuma Chapadera
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Chuma Chapadera
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Inu Ndinu Yehova
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Kodi Mumamva Bwanji?
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Ndinu Mphamvu Zathu, Chiyembekezo Chathu Komanso Timakudalirani
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 12

Nyimbo 147

Chuma Chapadera

(1 Petulo 2:9)

  1. Odzozedwa ndi mtundu,

    Watsopano wa M’lungu.

    Iye anawagula,

    Padziko lapansi.

    (KOLASI)

    N’chuma chapadera,

    Otchedwa dzina lanu

    Amakukondani.

    Amalengezadi za inu.

  2. Ndi mtundu woyeradi,

    Wophunzitsa cho’nadi.

    Mulungu wawapatsa

    Kuwala kwakedi.

    (KOLASI)

    N’chuma chapadera,

    Otchedwa dzina lanu

    Amakukondani.

    Amalengezadi za inu.

  3. Amasonkhanitsanso,

    Nkhosa zina mwakhama.

    Ndi okhulupirika.

    Kwa Mwanawankhosa.

    (KOLASI)

    N’chuma chapadera,

    Otchedwa dzina lanu

    Amakukondani.

    Amalengezadi za inu.

(Onaninso Yes. 43:20b; Mal. 3:17; Akol. 1:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena