Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 March tsamba 3
  • Muzitsatira Malamulo Awiri Aakulu Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzitsatira Malamulo Awiri Aakulu Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene “Kukonda Mulungu Kumatanthauza”
    Kodi Mungatani Kuti ‘Mulungu Apitirize Kukukondani’?
  • Chikondi Cha Mulungu Sichimatha
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
  • ‘Mulungu Anayesa Abulahamu’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Kodi Malamulo Khumi a Mulungu Ndi Chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 March tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 22-23

Muzitsatira Malamulo Awiri Aakulu Kwambiri

22:36-39

Pogwiritsa ntchito lemba la Mateyu 22:36-39, lembani manambala kuyambira ndi chifukwa chachikulu chimene timapitira kumisonkhano yathu:

  • Kuti tikalimbikitsidwe

  • Kuti tikalimbikitse ena

  • Kuti tikalambire komanso kusonyeza kuti timakonda Yehova

Msonkhano wa mpingo

N’chifukwa chiyani tiyenera kuyesetsa kupitabe kumisonkhano ngakhale titatopa kwambiri moti tikuona kuti sitingakapindule mokwanira?

Kodi ndi njira zina ziti zimene tingasonyezere kuti timamvera malamulo awiri aakulu kwambiri?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena