Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 March tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • NTCHITO YOGAWIRA KAPEPALA KOITANIRA ANTHU KU CHIKUMBUTSO (March 23–April 19):
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 March tsamba 1
M’bale wa ku South Africa akuonetsa vidiyo munthu amene amaphunzira naye Baibulo

Ku South Africa, akugwiritsa ntchito vidiyo pophunzira ndi munthu

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi cholinga cha Mulungu polenga anthu chinali chotani?

Lemba: Gen. 1:28

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi timadziwa bwanji kuti cholinga chomwe Mulungu analengera anthu chidzakwaniritsidwa?

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: Kodi timadziwa bwanji kuti cholinga chomwe Mulungu analengera anthu chidzakwaniritsidwa?

Lemba: Yes. 55:11

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi moyo udzakhala wotani Mulungu akadzakwaniritsa cholinga chomwe analengera anthu?

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi moyo udzakhala wotani Mulungu akadzakwaniritsa cholinga chomwe analengera anthu?

Lemba: Sal. 37:10, 11

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingatani kuti tidzalandire madalitso amene Mulungu analonjeza?

NTCHITO YOGAWIRA KAPEPALA KOITANIRA ANTHU KU CHIKUMBUTSO (March 23–April 19):

Tikukuitanani kumwambo wofunika kwambiri. Kapepala kanu ndi kameneka. Lachisanu pa 19 April, anthu mamiliyoni ambiri padziko lonse adzasonkhana kuti achite mwambo wokumbukira imfa ya Yesu Khristu. Kapepalaka kakusonyeza nthawi komanso malo omwe mwambowu udzachitikire m’dera lathu lino. Tikukuitananinso kuti mudzamvetsere nkhani ya mutu wakuti, “Yesetsani Kuti Mudzapeze Moyo Weniweni” yomwe idzakambidwe kutatsala mlungu umodzi kuti mwambowu uchitike.

Funso la Ulendo Wotsatira Ngati Munthuyo Wasonyeza Chidwi: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena