LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • od tsa. 213
  • Mlozela Nkhani

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mlozela Nkhani
  • Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova
Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova
od tsa. 213

Mlozela Nkhani

Cidziŵitso: Pa mlozela nkhani ali pansipa, nambala yoyamba ni mutu wa nkhani, yotsatila ni nambala ya ndime. Mwacitsanzo, pansi pa “Zilengezo” nkhani yoyamba imene alozako ni “zopeleka: 12:6.” Izi zitanthauza kuti nkhani yokhudza zopeleka ipezeka pa Mutu 12, ndime 6.

Akalinde: 11:14

Akhristu Ozilala: 8:26; 14:32

Akulu

abusa: 5:1-3; 14:7-12

amaikidwa mwa ndondomeko ya umulungu: 4:8

kukalamila: 5:22

kusunga ciyelo ca mpingo: 14:19-40

malo awo audindo: 5:25-36, 40

mamiting’i: 5:37

mgwilizano pakati pawo: 5:21

mmene tiyenela kuwaonela: 3:14; 5:38-39

okalamba kapena odwalila: 5:23-24

tumagulu na tumagulu toyesela: 9:42-44

ziyenelezo: 5:4-20

Alongo

ngati palibe abale oyenelezedwa: 6:9; 7:23

masukulu a zaumulungu: 10:17-18

utumiki wa mamangidwe: 10:21

Ana

abale acinyamata kukalamila: 6:14

kucita colakwa: 14:37

kupita patsogolo kuuzimu: 8:13-15; 10:26; masa. 179-181

kuthandiza makolo olemala komanso ambuye awo: 12:14

misonkhano: 7:2; 11:13-14

zocitika za kusukulu: 13:22-24

Anthu osauka: 12:12-15

Apainiya apadela: 10:11, 14, 17-18

Apainiya: 10:11-14

Apainiya othandiza: 10:11-12

Atumiki othandiza

kukalamila: 6:14

kuonetsa kuyamikila: 6:1-2, 15

nchito zawo: 6:7-12; 11:14

ziyenelezo: 6:3-6

Bungwe Lolamulila

kulidziŵa: 3:1-6

kuonetsa kuti timalidalila: 3:12-15

zifukwa zake tiyenela kutsatila zitsogozo zake: 3:9-11; 4:9-11

Cicilikizo ca ndalama

ca padziko lonse: 11:15; 12:2-4

dela: 12:8-11

mpingo: 11:6-7; 12:5-7

Cidzudzulo: 14:4, 23-24

Cikumbutso: 7:28-30

Colakwa

(Onaninso Kudzilekanitsa; Kucotsedwa mu mpingo; Kuika cizindikilo oyenda mosalongosoka; Kusemphana Maganizo; Kubwezeletsedwa)

ana: 14:37

cilengezo cake: 14:24, 29, 33, 39-40

colakwa cacikulu: 14:21-33

kulakwila Mkhristu wina: 14:5-6, 13-20

ofalitsa osabatizika: 14:38-40

Gawo

la kagulu komanso laumwini: 9:31-34

madela a zinenelo zosiyana-siyana: 9:36-37

zofunikila kulemba: 9:31

Gulu

gawo lakumwamba: 1:8-13

JW.ORG: 9:24-25

Kabuku ka Misonkhano ya Umoyo na Utumiki: 7:14-18

Kalembela: 5:27; 8:30

“Kapolo wokhulupilika ndi wanzelu”

kumudalila: 3:12-15

kumugonjela: 15:7

kumuzindikila: 3:4-6

Khadi ya Mpingo Yolembapo Nchito za Wofalitsa: 5:44; 8:10, 30

Komiti ya Utumiki

(Onani Komiti ya Utumiki ya Mpingo)

Komiti ya Utumiki ya Mpingo: 5:35

Kubwezeletsedwa: 14:34-36

Kucotsedwa Mumpingo: 14:25-29

Kudzilekanitsa: 14:30-33

Kudzipatulila na ubatizo

(Onani Ubatizo)

Kugonjela

(Onani Umutu)

Kuika cizindikilo oyenda mosalongosoka: 14:9-12

Kuikidwa kukhala mtumiki wa Mulungu: 8:3

Kukatumikila kosoŵa: 10:6-9

Kukhala acitsanzo cabwino

tanthauzo lake: 6:9

Kulalikila uthenga wabwino

acicepele: 8:13-15

kucitila lipoti: 8:19-29, 31-36

kufunika kwake: 9:5-8; 10:1-2

kukumana kotenga malangizo a ulaliki: 7:20-21

kulimbikitsa phunzilo la Baibo kulalikila mwamwayi: 8:5

kunyumba na nyumba: 9:3-9

kuseŵenzetsa jw.org: 9:24-25

kutsogolela: 5:3, 17, 29-33; 6:4

mabuku: 9:22-23

madela a zinenelo zosiyana-siyana: 9:35-44

magawo: 9:30-34

maonekedwe aumwini: 13:12

maulendo obwelelako: 9:14-15

mwamwayi: 9:26-29

ni nchito yocokela kwa Mulungu: 8:2

pa ciletso: 17:13-18

thandizo kwa munthu payekha: 5:28-29, 33; 7:21; 9:7, 15, 19

udindo wa woyang’anila utumiki: 5:28

ulaliki wa kagulu: 9:45-46

ulaliki wapoyela: 9:11-12

zaka za zana loyamba: 8:1-2; 9:1, 4

ziyenelezo: 8:6-9, 13-15

Kusemphana Maganizo

kuthetsa mavuto akulu-akulu: 14:13-20

kuthetsa mavuto ang’ono-ang’ono: 14:5-6

Mabuku

kusamalila zogwilitsila nchito: 12:16

madela a zinenelo zosiyana-siyana: 9:36, 38

ndalama zoyendetsela nchito yathu: 12:2-4

ni othandiza mu ulaliki: 9:22-23

Mabungwe alamulo: 4:12

Mabwalo a Misonkhano: 11:18-21

Madela a zinenelo zosiyana-siyana: 9:35-44

makalasi ophunzila cinenelo: 10:10

ngati mwininyumba akamba citundu cina: 9:38-41

tumagulu na tumagulu toyesela: 9:42-44

(Ma)komiti

Ya dziko: 5:53

Ya Nthambi: 4:13; 5:51-54

Ya Utumiki ya Mpingo: 5:35

yaciweluzo: 14:21-28, 34-37

Yolankhulana ndi Acipatala: 5:40

Yosamalila Nyumba ya Ufumu: 11:8

Makomiti aciweluzo: 14:21-28, 34-37

Makomiti Olankhulana ndi Acipatala, na Tumagulu Toyendela Odwala: 5:40

Malilo: 11:10-11

Malipoti

kufunika kwake: 8:19-22, 31-36

mukapita kwina: 8:30

ofalitsa: 5:34; 8:10, 23-29

oyang’anila madela: 5:46, 50; 9:44

Maphunzilo a Baibo

kucitila lipoti: 8:26

kulimbikitsa wophunzila kuti azilalikila mwamwayi: 8:5

kutsogolela wophunzila ku gulu: 9:20-21

zofunika: 9:16-17

Mavalidwe na kudzikongoletsa

atumiki othandiza: 6:5

awo amene amapatsidwa mwayi wapadela wotumikila: 6:9

kukaceza ku Beteli: 13:13

misonkhano: 11:12, 21

mu ulaliki: 13:12

zocitika zosangulutsa: 13:14

Mayeso, mayeselo: 13:4-5; 17:4-19

Mgonelo wa Ambuye: 7:28-30

Mgwilizanitsi wa Bungwe la Akulu

kucezela kwa woyang’anila dela: 5:42-44

kupenda maakaunti: 12:7

Msonkhano wa Umoyo na Utumiki: 7:18

ofalitsa atsopano: 8:8, 14

ofunsila ubatizo: 8:18; masa. 208-212

udindo wake: 5:26

Mgwilizano

akulu: 5:13, 21

kusunga mgwilizano: 17:20

madalitso: 4:15; 5:57; 13:30-31

maziko ake: 1:6-7; 13:28-29

pansi pa umutu wa Yesu: 2:9-11; 4:10-11

wa padziko lonse: 16:6-11

zopinga: 14:3; 17:6

Misonkhano

Aisiraeli: 11:1

akalinde: 11:14

akulu: 5:37

ana kupezekapo: 11:13

colinga: 7:1-2

kufunika kwake: 3:12; 7:4, 27; 15:7

kukambilana zamalonda: 13:27

kutenga malangizo a ulaliki: 7:20-21; 9:45

malo osonkhanila: 11:1-5, 18-19

misonkhano yacigawo: 7:25-26

misonkhano yadela: 7:24

mkati mwa kucezela kwa woyang’anila dela: 5:43, 47

nkhani ya anthu onse: 7:5-10

pamene mlongo atsogoza: 7:23

panthawi ya ciletso: 17:15-17

Phunzilo la Baibo la Mpingo: 7:17

Phunzilo la Nsanja ya Mlonda: 7:11-13

Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu: 7:14-19

Zaka za zana loyamba: 7:3; 11:2

Misonkhano Yacigawo: 7:25-27

Misonkhano Yadela

(Onani Msonkhano Wadela)

Mpingo

(Onaninso Nyumba ya Ufumu; Misonkhano)

mwa dongosolo la umulungu: 1:3; 4:4-11

umodzi: 13:28-30

watsopano ndiponso waung’ono: 7:22-23

Msonkhano wadela

kakonzedwe kake: 5:49

malo osonkhanila: 11:18

ndalama zoyendetsela: 12:8-11

Nchito yakuthupi: 13:25-26

Nkhani ya anthu onse: 7:5-10

Nyumba ya Ufumu

kuigwilitsila nchito mwapadela: 11:10-11

kuyeletsa na kusamalila: 11:7-8

kumanga: 10:21-23; 11:4-5, 15-17

kupatulila: 11:4

laibulali: 7:19

mipingo ingapo: 11:8-9

ndalama zogwilitsila nchito: 11:6; 12:5-6

Ofalitsa

(Onani Ofalitsa a mpingo; Ofalitsa Obatizika)

Ofalitsa a mpingo

(Onaninso Ofalitsa osabatizika)

acicepele: 8:13-14

kusamuka: 8:30

olemala: 8:29

thandizo kwa munthu payekha: 5:28-29, 33; 7:21; 9:7, 15, 19

watsopano: 8:5-6

ziyenelezo: 8:8

Ofalitsa osabatizika

ana: 8:13-15

colakwa: 14:38-40

pomanga Nyumba ya Ufumu kapena kuikonzanso: 11:17

ziyenelezo: 8:6-12

Ofesi ya Nthambi

mavalidwe na kudzikongoletsa pokaceza: 13:13

pamene kulumikizana nayo kwaduka: 17:15-17

udindo wake: 4:13

zopeleka ku: 12:2-4

Oimilako Likulu: 5:55-56

Oyang’anila

(Onani Akulu)

Phunzilo la Nsanja ya Mlonda: 7:11-13

Thandizo Pakagwa za Mwadzidzidzi: 12:15; 16:11

Tumagulu twa ulaliki

kugaŵila ku kagulu: 5:35

kukumana kotenga malangizo a ulaliki: 7:20-21

kuyeletsa nyumba ya Ufumu: 11:7

magawo: 9:31, 33

nchito za atumiki othandiza: 6:12

oyang’anila: 5:29-34

Ubatizo

ana: masa. 179-181

kuikidwa kukhala mtumiki: 8:3

ofalitsa osabatizika: masa. 182-184

pa misonkhano yadela, yacigawo: 7:24, 26

tanthauzo la: 8:16-18

mafunso okambilana: masa. 185-207

Ukhondo; Ciyelo

ciyelo ca kuthupi: 13:8-12

ciyelo m’makhalidwe, kuuzimu: 13:6-7

Nyumba ya Ufumu: 11:7-8

Umishonale: 10:15, 18

Umutu

m’banja: 15:9-10

m’gulu la Yehova: 1:9-10; 2:5, 9-10; 15:1-2

mu mpingo: 3:14; 4:15; 15:7

olamulila akulu-akulu: 15:11

Utumiki wa nchito ya mamangidwe: 10:21-23

Kagulu ka Mamangidwe: 10:23

mtumiki wa nchito ya mamangidwe wocokela ku dziko lina: 10:23

mtumiki wa nchito ya mamangidwe: 10:23

Wothandizila mu Dipatimenti ya Mapulani na Mamangidwe: 10:23

wothandizila pa nchito ya mamangidwe:10:23

Utumiki wa pa Beteli: 10:19-20

Woyang’anila dela

kucezela mipingo: 5:41-48

kufunsila kuti muwonjezele utumiki: 10:6, 10, 16, 20

kum’celeza: 5:50

ndiye amavomeleza kupempha mpingo watsopano: 7:22

tumagulu:9:44

Woyang’anila Utumiki: 5:28, 32; 9:31, 37, 45

Yehova Mulungu

kumuyandikila: 17:1-3

Mfumu ya Cilengedwe Conse: 15:1-4

Yesu Khristu

kugonjela Yehova: 15:5

M’busa Wabwino: 2:6; 5:1

Mkulu wa Ansembe: 2:4

Mtumiki: 8:1-2; 9:1

Mutu wa mpingo: 1:10; 2:5

Muwomboli: 2:3

Zigamulo: 12:6, 9, 11

Zikwati: 11:10-11

Zilengezo

cidzudzulo: 14:24

kubwezeletsa: 14:36

kucotsa mu mpingo: 14:29

ofalitsa osabatizika: 8:12; 14:39-40

zopeleka: 12:6

kudzilekanitsa: 14:33

Zocitika za kusukulu: 13:22-24

Zolinga

kudziikila zolinga zimene tingakwanitse: 8:37

kufunika kwake: 10:24-26

kukatumikila kumalo osoŵa: 10:6-9

kuphunzila cinenelo cina: 10:10

masukulu a zaumulungu: 10:17-18

nchito ya m’dela: 10:16

ofalitsa: 10:4-5

umishonale: 10:15

upainiya: 10:11-14

Utumiki wa pa Beteli: 10:19-20

utumiki wa mamangidwe: 10:21-23

Zopeleka: 3:13; 11:6-7, 15; 12:2-11

Zosangulutsa na zosangalatsa: 13:15-21

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani