LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 1/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 1/15 masa. 1-2

Zamkati

January 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

MARCH 2-8, 2015

Yamikani Yehova Ndipo Mudzadalitsidwa

TSAMBA 8 • NYIMBO: 2, 75

MARCH 9-15, 2015

Cifukwa Cake Timacita Mgonelo wa Ambuye

TSAMBA 13 • NYIMBO: 8, 109

MARCH 16-22, 2015

Khalani ndi Banja Lolimba ndi Lacimwemwe

TSAMBA 18 • NYIMBO: 36, 51

MARCH 23-29, 2015

Lolani Yehova Kulimbitsa ndi Kuteteza Cikwati Canu

TSAMBA 23 • NYIMBO: 87, 50

MARCH 30, 2015–APRIL 5, 2015

Kodi N’zotheka Kukhala m’Cikondi Ceniceni?

TSAMBA 28 • NYIMBO: 72, 63

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Yamikani Yehova Ndipo Mudzadalitsidwa

Tikamasinkhasinkha ndi kuyamikila zinthu zabwino zimene Yehova waticitila, tidzakhala ndi mzimu woyamikila. Kukhala ndi mtima woyamikila kudzatithandiza kugonjetsa mzimu wosafuna kuyamikila ndipo tidzapilila mayeselo. Lemba lathu la caka ca 2015 lidzatikumbutsa za mfundo imeneyi kwa caka conse.

▪ Cifukwa Cake Timacita Mgonelo wa Ambuye

Nkhani imeneyi itionetsa bwino cifukwa cake tiyenela kucita mwambo wokumbukila imfa ya Yesu. Idzafotokoza cimene mkate ndi vinyo zimene timagwilitsila nchito pa Cikumbutso zimaimila. Idzafotokozanso mmene munthu amadziŵila kuti ayenela kudya zizindikilo zimenezo. Nkhaniyi idzatithandiza kuona zimene aliyense wa ife ayenela kucita pokonzekela Mgonelo wa Ambuye.

▪ Khalani ndi Banja Lolimba ndi Lacimwemwe

▪ Lolani Yehova Kulimbitsa ndi Kuteteza Cikwati Canu

Amene ali pa banja akulimbana ndi mavuto ndi mayeselo ambili. Koma ndi thandizo la Yehova, n’zotheka kukhala ndi cikwati colimba ndi cacimwemwe. Nkhani yoyamba idzafotokoza njila zisanu zimene zingathandize cikwati kukhala colimba ndi cokhalitsa, ndiponso cimene cingathandize okwatilanawo kuti asalekane. Nkhani yaciŵili idzafokoza zinthu zimene okwatilana ayenela kucita kuti cikwati cao cikhale colimba mwakuuzimu.

▪ Kodi N’zotheka Kukhala m’Cikondi Ceniceni?

Kodi cikondi ceniceni cimene cimakhala pakati pa mwamuna ndi mkazi n’cotani? Kodi n’zotheka kukhala m’cikondi ceniceni? Kodi cikondi cimeneco cingasonyezedwe bwanji? Dziŵani zimene Nyimbo ya Solomo imatiphunzitsa ponena za cikondi ceniceni.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Anadzipeleka Mofunitsitsa—Ku New York

PA CIKUTO: Akulalikila atagwila Baibulo m’manja, mumzinda wokongola wocedwa Grindelwald, ndipo mapili amene akuonekela ca kumbuyo amacedwa Bernese Alps

SWITZERLAND

KULI ANTHU

7,876,000

OFALITSA

18,646

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2013)

31,980

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani