LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 February tsa. 2
  • Kumvela Yehova Kumabweletsa Madalitso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kumvela Yehova Kumabweletsa Madalitso
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • N’zotheka Kupeza Nzelu
    Galamuka!—2021
  • Yehova Amakwanilitsa Malonjezo Ake Nthawi Zonse
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Anthu a Yehova Amakonda Cilungamo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kondani Cilungamo, Danani Nako Kusamvela Malamulo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 February tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YESAYA 47-51

Kumvela Yehova Kumabweletsa Madalitso

48:17

  • Mwacikondi Yehova amationetsa ‘njila imene tiyenela kuyendamo’ kuti tikondwele na umoyo. Tikamumvela zinthu zimatiyendela bwino.

“Mtendele . . . udzakhala ngati mtsinje”

48:18

  • Yehova akulonjeza bata na mtendele woculuka woyendelela monga mtsinje.

“Cilungamo . . . cidzakhala ngati mafunde a m’nyanja”

  • Zocita zathu zacilungamo zingakhale zosaŵelengeka monga mafunde a m’nyanja

Mtsinje umene ukuyendelela ndi mafunde a m’nyanja
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani