LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsa. 7
  • Nkhani Yatsopano Imene Izipezeka mu Nsanja ya Olonda

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nkhani Yatsopano Imene Izipezeka mu Nsanja ya Olonda
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Nkhani Zofanana
  • Limbikitsani Kuyambitsa Maphunzilo a Baibo pa Ciŵelu Coyamba
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Zothandiza mu Ulaliki
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Moseŵenzetsela Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsa. 7

Nkhani Yatsopano Imene Izipezeka mu Nsanja ya Olonda

Pa Ciŵelu coyamba ca mwezi uliwonse, takhala tikugwilitsila nchito nkhani ya mu Nsanja ya Olonda yakuti “Phunzilani Zimene Mau a Mulungu Amanena,” poyambitsa maphunzilo a Baibo. Koma kuyambila mu January, nkhani imeneyi idzaloŵedwa m’malo ndi nkhani yakuti “Mafunso a m’Baibo Ayankhidwa,” imene idzayamba kupezeka patsamba lothela la Nsanja ya Olonda yogaŵila. Tingagwilitsile nchito nkhani yakuti “Mafunso a m’Baibo Ayankhidwa” mu ulaliki monga mmene tinali kugwilitsila nchito nkhani yakuti, “Phunzilani Zimene Mau a Mulungu Amanena.” (km 12/10 tsa. 2) Monga zinalili kale, Utumiki Wathu wa Ufumu uzikhala ndi ulaliki wacitsanzo umene tingagwilitsile nchito pa Ciŵelu coyamba ca mwezi.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani