LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsa. 3
  • Zimene Tiphunzilapo pa Ulaliki wa Yesu wa pa Phili

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Tiphunzilapo pa Ulaliki wa Yesu wa pa Phili
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • 5:3
  • Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Kodi Mukutumikila Yehova Mosalekeza?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Anapitiliza Kulankhula Mawu a Mulungu Molimba Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Kodi Munadzifunsapo?
    Galamuka!—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 January tsa. 3
Opempha-pempha

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MATEYU 4-5

Zimene Tiphunzilapo pa Ulaliki wa Yesu wa pa Phili

5:3

Kodi mumazindikila zosoŵa zanu zauzimu?

Wacicepele amwetulila

Mau akuti “anthu amene amazindikila zosoŵa zawo zauzimu,” atanthauza anthu opempha-pempha mzimu wa Mulungu. (Mat. 5:3.) Tingaonetse kuti ndise ofunitsitsa kulandila thandizo lauzimu locokela kwa Mulungu mwa. . .

  • kuŵelenga Baibo tsiku lililonse

  • kumakonzekela misonkhano na kupezekapo

  • kuŵelenga zofalitsa zathu, ndipo ngati n’zotheka, kumaŵelenganso nkhani zina zopezeka pa webusaiti yathu

  • kumatamba pulogilamu ya JW Broadcasting ya mwezi uliwonse

Ningakulitse bwanji cizoloŵezi ca kumadya cakudya cauzimu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani