Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 35:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ana aamuna amene Leya anaberekera Yakobo anali Rubeni+ mwana wake woyamba, Simiyoni, Levi, Yuda, Isakara ndi Zebuloni.

  • Genesis 46:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana a Isakara+ anali Tola,+ Puva,+ Yabi ndi Simironi.+

  • Genesis 49:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Isakara+ ndi bulu wa mafupa olimba, amagona pansi atasenza matumba a katundu uku ndi uku.

  • Deuteronomo 33:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kwa Zebuloni anati:+

      “Kondwera Zebuloni iwe, pa maulendo ako,+

      Ndiponso iwe Isakara, m’mahema ako.+

  • 1 Mbiri 12:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 A fuko la Isakara,+ amene anali ndi nzeru zotha kudziwa nthawi,+ ndi zimene Aisiraeli ayenera kuchita,+ analipo atsogoleri 200, ndipo iwo anali kulamulira abale awo onse.

  • Chivumbulutso 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mu fuko la Simiyoni,+ 12,000.

      Mu fuko la Levi,+ 12,000.

      Mu fuko la Isakara,+ 12,000.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena