1 Mafumu 1:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Wansembe Zadoki,+ mneneri Natani,+ Benaya+ mwana wa Yehoyada, Akereti+ ndi Apeleti+ anatsetsereka n’kukakweza Solomo panyulu yaikazi ya Mfumu Davide,+ kenako anapita naye ku Gihoni.+ Esitere 6:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Pamenepo Hamani anatenga chovala+ ndi hatchi, ndipo chovalacho anaveka Moredekai.+ Kenako anam’kwezeka pahatchiyo ndi kumuyendetsa m’bwalo+ la mzinda, akufuula pamaso pake kuti:+ “Umu ndi mmene timachitira ndi munthu amene mfumu yafuna kum’patsa ulemu.”+
38 Wansembe Zadoki,+ mneneri Natani,+ Benaya+ mwana wa Yehoyada, Akereti+ ndi Apeleti+ anatsetsereka n’kukakweza Solomo panyulu yaikazi ya Mfumu Davide,+ kenako anapita naye ku Gihoni.+
11 Pamenepo Hamani anatenga chovala+ ndi hatchi, ndipo chovalacho anaveka Moredekai.+ Kenako anam’kwezeka pahatchiyo ndi kumuyendetsa m’bwalo+ la mzinda, akufuula pamaso pake kuti:+ “Umu ndi mmene timachitira ndi munthu amene mfumu yafuna kum’patsa ulemu.”+