Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 105:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kumeneko anasautsa mapazi ake ndi matangadza,+

      Anam’manga ndi maunyolo.+

  • Salimo 107:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Koma akuteteza munthu wosauka ku nsautso,+

      Ndipo akumuchulukitsa kukhala mabanja ambiri ngati gulu la nkhosa.+

  • Amosi 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Inu mukumwera vinyo m’makapu akuluakulu+ ndipo mukudzola mafuta apamwamba kwambiri+ komanso simunamve ululu pamene tsoka linagwera Yosefe.+

  • Machitidwe 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 ndipo anamulanditsa m’masautso ake onse. Anamupatsanso chisomo ndi nzeru pamaso pa Farao mfumu ya Iguputo. Ndipo anamuika kuti ayang’anire Iguputo ndi nyumba yonse ya Farao.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena