Genesis 35:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Pomalizira pake, pamene moyo wake+ unali kutayika (pakuti anamwalira),+ anatcha mwanayo dzina lakuti Beni-oni.* Koma bambo ake anamutcha Benjamini.*+ Genesis 42:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Komabe bambo awo anati: “Zoti mwana wanga apite nanu, izo ndakana, chifukwa m’bale wake anafa, ndipo iye anatsala yekha.+ Ngati angakumane ndi tsoka n’kufa panjira, ndithu mudzatsitsira ku Manda+ imvi zanga ndi chisoni.” Genesis 43:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma iwo anayankha kuti: “Munthuyo anachita kufunsa za ife ndi banja lathu kuti, ‘Kodi bambo anu akali ndi moyo?+ Kodi muli ndi m’bale wanu wina?’ Ndipo ife tinayankha mogwirizana ndi zimene anafunsa.+ Nanga tikanadziwa bwanji zoti anena kuti, ‘Mukam’bweretse kuno m’bale wanuyo’?”+
18 Pomalizira pake, pamene moyo wake+ unali kutayika (pakuti anamwalira),+ anatcha mwanayo dzina lakuti Beni-oni.* Koma bambo ake anamutcha Benjamini.*+
38 Komabe bambo awo anati: “Zoti mwana wanga apite nanu, izo ndakana, chifukwa m’bale wake anafa, ndipo iye anatsala yekha.+ Ngati angakumane ndi tsoka n’kufa panjira, ndithu mudzatsitsira ku Manda+ imvi zanga ndi chisoni.”
7 Koma iwo anayankha kuti: “Munthuyo anachita kufunsa za ife ndi banja lathu kuti, ‘Kodi bambo anu akali ndi moyo?+ Kodi muli ndi m’bale wanu wina?’ Ndipo ife tinayankha mogwirizana ndi zimene anafunsa.+ Nanga tikanadziwa bwanji zoti anena kuti, ‘Mukam’bweretse kuno m’bale wanuyo’?”+