Genesis 43:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Pobwerera, zinachitika n’zakuti, titafika pamalo ogona+ n’kumasula matumba athu, tinangoona kuti ndalama za aliyense zili pakamwa pa thumba lake, zonse malinga ndi kulemera kwake. Choncho tabwera nazo kuti tizibweze tokha.+ Miyambo 12:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Wolungama amasamalira moyo wa chiweto chake,+ koma chisamaliro cha anthu oipa n’chankhanza.+ Yeremiya 9:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndikanakonda kukhala ndi malo a m’chipululu ogona anthu apaulendo.+ Pamenepo ndikanasiya anthu anga ndi kuwachokera, pakuti onsewo ndi achigololo,+ gulu la anthu ochita zachinyengo.+ Yeremiya 41:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Iwo anakakhala kumalo ogona a Chimamu pafupi ndi Betelehemu+ ndi cholinga choti apitirize ulendo wawo kukalowa mu Iguputo.+
21 Pobwerera, zinachitika n’zakuti, titafika pamalo ogona+ n’kumasula matumba athu, tinangoona kuti ndalama za aliyense zili pakamwa pa thumba lake, zonse malinga ndi kulemera kwake. Choncho tabwera nazo kuti tizibweze tokha.+
2 Ndikanakonda kukhala ndi malo a m’chipululu ogona anthu apaulendo.+ Pamenepo ndikanasiya anthu anga ndi kuwachokera, pakuti onsewo ndi achigololo,+ gulu la anthu ochita zachinyengo.+
17 Iwo anakakhala kumalo ogona a Chimamu pafupi ndi Betelehemu+ ndi cholinga choti apitirize ulendo wawo kukalowa mu Iguputo.+