Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mukhale nafe kwathu kuno, dziko lino likhalanso lanu. Mukhazikike, ndipo muzichita malonda mwaufulu.”+

  • Genesis 42:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno mukabweretse mng’ono wanuyo kwa ine. Mukatero, ndidzatsimikiza kuti mukunena zoona, ndipo simudzaphedwa.”+ Iwo anavomereza kuchita zimenezo.

  • Yakobo 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tamverani tsopano inu amene mumati: “Lero kapena mawa tipita kumzinda wakutiwakuti ndipo tikatha chaka kumeneko. Tikachita malonda kumeneko ndi kupeza phindu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena