Genesis 45:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Atafika, anauza bambo awo kuti: “Yosefe uja ali moyo! Ndiye woyang’anira dziko lonse la Iguputo!”+ Yakobo atamva zimenezo sizinam’khudze chifukwa sanazikhulupirire.+ Machitidwe 7:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 ndipo anamulanditsa m’masautso ake onse. Anamupatsanso chisomo ndi nzeru pamaso pa Farao mfumu ya Iguputo. Ndipo anamuika kuti ayang’anire Iguputo ndi nyumba yonse ya Farao.+ 1 Yohane 4:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Komanso ife taona+ ndipo tikuchitira umboni+ kuti Atate anatumiza Mwana wake kuti akhale Mpulumutsi wa dziko.+
26 Atafika, anauza bambo awo kuti: “Yosefe uja ali moyo! Ndiye woyang’anira dziko lonse la Iguputo!”+ Yakobo atamva zimenezo sizinam’khudze chifukwa sanazikhulupirire.+
10 ndipo anamulanditsa m’masautso ake onse. Anamupatsanso chisomo ndi nzeru pamaso pa Farao mfumu ya Iguputo. Ndipo anamuika kuti ayang’anire Iguputo ndi nyumba yonse ya Farao.+
14 Komanso ife taona+ ndipo tikuchitira umboni+ kuti Atate anatumiza Mwana wake kuti akhale Mpulumutsi wa dziko.+