Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 42:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Komabe bambo awo anati: “Zoti mwana wanga apite nanu, izo ndakana, chifukwa m’bale wake anafa, ndipo iye anatsala yekha.+ Ngati angakumane ndi tsoka n’kufa panjira, ndithu mudzatsitsira ku Manda+ imvi zanga ndi chisoni.”

  • Genesis 44:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Koma mmodzi wa awiriwo anandisiya, ndipo ndinafuula kuti: “Kalanga ine! Ndithu wakhadzulidwa mwana wanga!”+ Mpaka lero sindinamuonenso.

  • Luka 24:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma kwa iwo, zimene anali kuwauzazo zinali zopanda pake ndipo sanawakhulupirire amayiwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena