Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Iwo anamuonera patali akubwera, ndipo asanafike pafupi anayamba kupangana chiwembu choti amuphe.+

  • Genesis 45:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma musadzimvere chisoni+ kapena kudzipsera mtima kuti munandigulitsa kuno. Mulungu ndiye ananditumiza patsogolo panu kuti ndidzapulumutse miyoyo yanu.+

  • Salimo 105:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mulungu anatsogoza munthu kuti anthu akewo abwere pambuyo pake,

      Anatumiza Yosefe amene anagulitsidwa kuti akhale kapolo.+

  • Salimo 119:71
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  71 Zili bwino kuti ndasautsika,+

      Kuti ndiphunzire malamulo anu.+

  • Aroma 8:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tikudziwa tsopano kuti Mulungu amagwirizanitsa zochita zake zonse+ pofuna kupindulitsa amene amakonda Mulungu, anthu oitanidwa mogwirizana ndi cholinga chake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena