Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 47:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Iwo anayankha kuti: “Mwapulumutsa miyoyo yathu.+ Mwatikomera mtima mbuyathu, ndipo tidzakhala akapolo a Farao.”+

  • Genesis 50:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Inu munali ndi cholinga chondichitira zoipa. Koma Mulungu anali ndi cholinga chabwino, kuti apulumutse miyoyo ya anthu ambiri ngati mmene akuchitira panomu.+

  • 1 Samueli 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova ndi Wakupha ndi Wosunga moyo,+

      Iye ndi Wotsitsira Kumanda,+ ndiponso Woukitsa.+

  • Salimo 33:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kuti apulumutse moyo wawo ku imfa,+

      Ndi kuwasunga ndi moyo pa nthawi ya njala.+

  • Salimo 105:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mulungu anatsogoza munthu kuti anthu akewo abwere pambuyo pake,

      Anatumiza Yosefe amene anagulitsidwa kuti akhale kapolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena