Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zikanakhala bwino mukanandibisa m’Manda,+

      Mukanandibisa mpaka mkwiyo wanu utachoka,

      Mukanati mundiikire nthawi+ n’kudzandikumbukira.+

  • Salimo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, mwanditulutsa m’Manda,+

      Mwandisunga ndi moyo, kuti ndisatsikire m’dzenje.+

  • Salimo 49:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma Mulungu adzawombola moyo wanga ku Manda,+

      Pakuti adzandilandira. [Seʹlah.]

  • Salimo 86:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti kukoma mtima kosatha kumene mwandisonyeza ndi kwakukulu,+

      Ndipo mwapulumutsa moyo wanga ku Manda, kumalo apansi penipeni.+

  • Yohane 11:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Marita anati: “Ndikudziwa kuti adzauka pa kuuka kwa akufa+ m’tsiku lomaliza.”

  • 1 Akorinto 15:55
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 “Imfa iwe, kupambana kwako kuli kuti? Imfawe, mphamvu yako ili kuti?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena