Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Loti anawaumiriza kwambiri+ moti mpaka iwo anapita naye kunyumba kwake. Kumeneko anawakonzera phwando,+ n’kuwaphikira mikate yopanda chofufumitsa,+ ndipo anadya.

  • Ekisodo 12:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Ndiyeno ufa wokanda umene anachoka nawo ku Iguputo uja anayamba kuuphika mikate yozungulira yopanda chofufumitsa, chifukwa ufa wokandawo unalibe zofufumitsa. Ufawo unalibe zofufumitsa chifukwa chakuti anawapitikitsa ku Iguputo ndipo anachoka mofulumira kwambiri. Komanso iwo anaphika mikateyo chifukwa chakuti sanathe kukonza chakudya chilichonse ponyamuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena