Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anamudyetsanso mafuta a mkaka wa ng’ombe ndi mkaka wa nkhosa,+

      Pamodzi ndi mafuta a nkhosa.

      Anamudyetsa nkhosa zamphongo za ku Basana, mbuzi zamphongo,+

      Pamodzi ndi tirigu wabwino koposa ngati mafuta okuta impso.+

      Ndipo anali kumwa magazi a mphesa monga vinyo.+

  • 2 Samueli 17:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Iwo anabweretsanso uchi,+ mafuta a mkaka,+ wa ng’ombe ndiponso nkhosa. Anabweretsa zinthu zimenezi kuti Davide ndi anthu onse amene anali naye adye.+ Iwo anali kunena kuti: “Anthu amenewa ali ndi njala, atopa ndipo ali ndi ludzu m’chipululu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena