-
2 Samueli 11:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Ndiyeno mthengayo anauza Davide kuti: “Amunawo anakula mphamvu kuposa ife, moti anatuluka kudzamenyana nafe kuthengo, koma tinayesetsa kuwapanikiza mpaka kuchipata cha mzinda.
-