Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 40:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako udzatchinge bwalo+ la chihema chopatulika ndi mpanda, ndipo pachipata cha bwalolo udzakolowekepo nsalu yake yotchinga.+

  • 1 Mafumu 6:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kenako anamanga khoma la miyala yosema lotalika mizere itatu+ kuzungulira bwalo lamkati,+ ndipo anawonjezeranso mzere umodzi wa matabwa a mkungudza.

  • 1 Mafumu 8:64
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 64 Tsiku limenelo, pakati pa bwalo la nyumba ya Yehova+ panayenera kupatulidwa ndi mfumu, chifukwa inafunika kuperekerapo nsembe yopsereza, nsembe yambewu, ndi mafuta a nsembe zachiyanjano. Inatero popeza guwa lansembe lamkuwa+ limene lili pamaso pa Yehova linachepa, ndipo nsembe yopsereza, nsembe yambewu, ndi mafuta+ a nsembe zachiyanjano sizikanakwanapo.

  • Salimo 84:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti kukhala tsiku limodzi m’mabwalo anu n’kwabwino kuposa kukhala masiku 1,000 kwina.+

      Ndasankha kuima pakhomo la nyumba ya Mulungu wanga+

      Kuposa kukhala m’mahema a anthu oipa.+

  • Salimo 92:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Anthu obzalidwa m’nyumba ya Yehova,+

      M’mabwalo a Mulungu wathu,+ adzakula mosangalala.

  • Salimo 100:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Lowani pazipata zake ndi mawu oyamikira,+

      Lowani m’mabwalo ake ndi mawu otamanda.+

      Muyamikeni, tamandani dzina lake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena