Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Alipo amene sanakonderepo akalonga,

      Ndipo saganizira kwambiri wolemekezeka kuposa wonyozeka,+

      Chifukwa onsewo anapangidwa ndi manja ake.+

  • Miyambo 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Munthu wolemera ndiponso munthu wosauka n’chimodzimodzi.+ Amene anapanga onsewa ndi Yehova.+

  • Aefeso 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Inu ambuye, muzichitiranso akapolo anu chimodzimodzi ndipo muleke kuwaopseza,+ pakuti mukudziwa kuti Ambuye wa nonsenu, wa iwowo ndi wa inuyo,+ ali kumwamba ndipo alibe tsankho.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena