Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 27:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Upange guwa lansembe la matabwa a mthethe, m’litali mikono isanu, ndipo m’lifupi mikono isanu. Guwalo+ likhale lofanana muyezo wake mbali zake zonse zinayi, ndipo msinkhu wake likhale mikono itatu.

  • Ekisodo 40:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Udzadzozenso guwa lansembe zopsereza ndi ziwiya zake zonse ndi kuliyeretsa.+ Pamenepo guwalo lidzakhala lopatulika kwambiri.+

  • Aheberi 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ife tili ndi guwa lansembe limene ochita utumiki wopatulika kuchihema, alibe ulamuliro wodya za paguwapo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena