Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 “Upangenso kachitsulo konyezimira kaphanthiphanthi kagolide woyenga bwino, ndipo ulembepo mochita kugoba ngati mmene amagobera chidindo, mawu akuti, ‘Chiyero n’cha Yehova.’+

  • Levitiko 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Anamuvekanso nduwira+ pamutu pake, n’kuika patsogolo pa nduwirayo kachitsulo konyezimira kaphanthiphanthi kagolide, chizindikiro chopatulika cha kudzipereka,+ monga mmene Yehova analamulira Mose.

  • Zekariya 14:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Pa tsiku limenelo, pamabelu a mahatchi padzalembedwa mawu+ akuti ‘Chiyero n’cha Yehova!’+ Ndipo miphika yakukamwa kwakukulu+ ya m’nyumba ya Yehova adzaigwiritsa ntchito ngati mbale zolowa+ za paguwa lansembe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena