Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma mtundu umene adzautumikirewo ndidzauweruza.+ Pambuyo pake, iwo adzachokako ndi katundu wochuluka.+

  • Ekisodo 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chotero ndidzachititsa Aiguputo kukomera mtima anthu anga, moti pochoka simudzachoka chimanjamanja.+

  • Ekisodo 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano uza anthu kuti mwamuna aliyense ndi mkazi aliyense apemphe kwa mnzake zinthu zasiliva ndi zagolide.”+

  • Salimo 105:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Ndiyeno anayamba kuwatulutsa atatenga siliva ndi golide.+

      Pakati pa mafuko ake panalibe amene anapunthwa panjira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena