Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yehova anatumiza munthu wina, mneneri,+ kwa ana a Isiraeli, ndipo anawauza kuti: “Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena kuti, ‘Ndine amene ndinakutulutsani mu Iguputo,+ m’nyumba yaukapolo.+

  • 1 Samueli 2:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ndiyeno munthu wa Mulungu+ anapita kwa Eli ndi kumuuza kuti: “Yehova wanena kuti, ‘Kodi ine sindinadzisonyeze kunyumba ya kholo lako pamene anali akapolo kunyumba ya Farao ku Iguputo?+

  • 1 Samueli 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Komanso, mukuumitsiranji mitima yanu mmene Aiguputo ndi Farao anaumitsira mitima yawo?+ Si paja Mulungu atangowakhaulitsa+ analola Aisiraeli kupita, ndipo iwo anapitadi?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena